Masalimo 36:4 - Buku Lopatulika4 Alingirira zopanda pake pakama pake; adziika panjira posati pabwino; choipa saipidwa nacho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Alingirira zopanda pake pakama pake; adziika panjira posati pabwino; choipa saipidwa nacho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Amaganiza zachiwembu akamagona usiku. Amayenda pa njira imene siili yabwino, sapewa zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ngakhale ali pa bedi pake amakonzekera zoyipa; iye amadzipereka yekha ku njira ya uchimo ndipo sakana cholakwa chilichonse. Onani mutuwo |