Masalimo 36:5 - Buku Lopatulika5 Yehova, m'mwamba muli chifundo chanu; choonadi chanu chifikira kuthambo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Yehova, m'mwamba muli chifundo chanu; choonadi chanu chifikira kuthambo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Inu Chauta, chikondi chanu chosasinthika chimafika mpaka kumwamba, kukhulupirika kwanu kumafika mpaka ku mitambo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Chikondi chanu Yehova, chimafika ku mayiko a kumwamba, kukhulupirika kwanu mpaka ku mitambo. Onani mutuwo |