Masalimo 36:6 - Buku Lopatulika6 Chilungamo chanu chikunga mapiri a Mulungu; maweruzo anu akunga chozama chachikulu, Yehova, musunga munthu ndi nyama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Chilungamo chanu chikunga mapiri a Mulungu; maweruzo anu akunga chozama chachikulu, Yehova, musunga munthu ndi nyama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kulungama kwanu kumaonekera ngati mapiri aatali, kuweruza kwanu nkozama ngati nyanja yakuya, Inu Chauta, mumasamalira anthu ndi nyama zomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Chilungamo chanu Mulungu chili ngati mapiri aakulu, chiweruzo chanu chili ngati kuzama kwakukulu. Yehova mumasunga munthu pamodzi ndi chinyama. Onani mutuwo |