Masalimo 18:32 - Buku Lopatulika32 Mulungu ndiye wondizingiza mphamvu m'chuuno, nakonza njira yanga ikhale yangwiro. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Mulungu ndiye wondizingiza mphamvu m'chuuno, nakonza njira yanga ikhale yangwiro. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Mulungu wathu ndiye amene amandiveka mphamvu, wandichotsera zoopsa m'njira zanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Ndi Mulungu amene anandipatsa mphamvu ndi kulungamitsa njira yanga. Onani mutuwo |