Masalimo 18:33 - Buku Lopatulika33 Alinganiza mapazi anga ngati a mbawala, nandiimitsa pamsanje panga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Alinganiza mapazi anga ngati a mbawala, nandiimitsa pamsanje panga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Amalimbitsa miyendo yanga ngati ya mbaŵala, ndipo amandisunga bwino m'mapiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Iye amasandutsa mapazi anga kukhala ngati ambawala yayikazi; Iye amandithandiza kuyimirira pamwamba pa mapiri. Onani mutuwo |