Masalimo 18:31 - Buku Lopatulika31 Pakuti Mulungu ndani wosati Yehova? Ndipo thanthwe ndani wosati Mulungu wathu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Pakuti Mulungu ndani wosati Yehova? Ndipo thanthwe ndani wosati Mulungu wathu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Palibe mulungu wina koma Chauta yekha. Palibe thanthwe lina lothaŵirapo koma Mulungu wathu yekha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Mulungu wina ndi uti wofanana nanu Yehova? Ndipo ndani amene ndi Thanthwe kupatula Mulungu wathu? Onani mutuwo |