Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 34:19 - Buku Lopatulika

19 Masautso a wolungama mtima achuluka, koma Yehova amlanditsa mwa onsewa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Masautso a wolungama mtima achuluka, koma Yehova amlanditsa mwa onsewa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Anthu a Mulungu amaona masautso ambiri. Komabe Chauta amawapulumutsa m'mavuto awo onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Munthu wolungama atha kukhala ndi mavuto ambiri, Koma Yehova amamulanditsa ku mavuto onsewo,

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 34:19
24 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anadalitsa chitsiriziro cha Yobu koposa chiyambi chake, ndipo anali nazo nkhosa zikwi khumi ndi zinai, ndi ngamira zikwi zisanu ndi chimodzi, ndi ng'ombe zamagoli chikwi chimodzi, ndi abulu aakazi chikwi chimodzi.


Adzakupulumutsa m'masautso asanu ndi limodzi; chinkana mwa asanu ndi awiri palibe choipa chidzakukhudza.


Achiritsa osweka mtima, namanga mabala ao.


Iwowo anaitana, ndipo Yehova anawamva, nawalanditsa kumasautso ao onse.


Ndinafuna Yehova ndipo anandivomera, nandilanditsa m'mantha anga onse.


Munthu uyu wozunzika anafuula, ndipo Yehova anamumva, nampulumutsa m'masautso ake onse.


Pamenepo mudzakondwera nazo nsembe zachilungamo, ndi nsembe yopsereza ndi yopsereza yathunthu; pamenepo adzapereka ng'ombe paguwa lanu la nsembe.


Inu, amene munationetsa nsautso zambiri ndi zoipa, mudzatipatsanso moyo, ndi kutitenganso munsi mwa dziko.


Pakuti wolungama amagwa kasanu ndi kawiri, nanyamukanso; koma oipa akhumudwa pomfikira tsoka.


Funani Yehova popezeka Iye, itanani Iye pamene ali pafupi;


Pakuti atero Iye amene ali wamtali wotukulidwa, amene akhala mwachikhalire, amene dzina lake ndiye Woyera, Ndikhala m'malo aatali ndi oyera, pamodzi ndi yense amene ali wa mzimu wosweka ndi wodzichepetsa, kutsitsimutsa mzimu wa odzichepetsa, ndi kutsitsimutsa mtima wa osweka.


Zinthu izi ndalankhula ndi inu, kuti mwa Ine mukakhale nao mtendere. M'dziko lapansi mudzakhala nacho chivuto, koma limbikani mtima; ndalingonjetsa dziko lapansi Ine.


nalimbikitsa mitima ya ophunzira, nadandaulira iwo kuti akhalebe m'chikhulupiriro, ndi kuti tiyenera kulowa mu ufumu wa Mulungu ndi zisautso zambiri.


Pakuti chisautso chathu chopepuka cha kanthawi chitichitira ife kulemera koposa kwakukulu ndi kosatha kwa ulemerero;


Ndipo Elimeleki mwamuna wake wa Naomi anamwalira; natsala iye ndi ana ake awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa