Masalimo 34:19 - Buku Lopatulika19 Masautso a wolungama mtima achuluka, koma Yehova amlanditsa mwa onsewa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Masautso a wolungama mtima achuluka, koma Yehova amlanditsa mwa onsewa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Anthu a Mulungu amaona masautso ambiri. Komabe Chauta amawapulumutsa m'mavuto awo onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Munthu wolungama atha kukhala ndi mavuto ambiri, Koma Yehova amamulanditsa ku mavuto onsewo, Onani mutuwo |