Masalimo 17:15 - Buku Lopatulika15 Koma ine ndidzapenyerera nkhope yanu m'chilungamo, ndidzakhuta mtima ndi maonekedwe anu, pamene ndidzauka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma ine ndidzapenyerera nkhope yanu m'chilungamo, ndidzakhuta mtima ndi maonekedwe anu, pamene ndidzauka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Koma ine m'kulungama kwanga ndidzaona nkhope yanu. Tsono ine nditadzuka, ndidzakondwa kotheratu poonana ndi Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndipo ine mʼchilungamo ndidzaona nkhope yanu; pamene ndidzadzuka, ndidzakondwera kwambiri poonana nanu. Onani mutuwo |