Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 13:6 - Buku Lopatulika

Ndidzaimbira Yehova, pakuti anandichitira zokoma.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndidzaimbira Yehova, pakuti anandichitira zokoma.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndidzaimbira Chauta, popeza kuti wandichitira zabwino.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine ndidzayimbira Yehova pakuti wandichitira zokoma.

Onani mutuwo



Masalimo 13:6
5 Mawu Ofanana  

Ubwere moyo wanga ku mpumulo wako; pakuti Yehova anakuchitira chokoma.


Ndidzakuyamikani ndi mtima woongoka, pakuphunzira maweruzo anu olungama.


Kwezekani, Yehova, mu mphamvu yanu; potero tidzaimba ndi kulemekeza chilimbiko chanu.


Yehova ndiye mphamvu yanga, ndi chikopa changa; mtima wanga wakhulupirira Iye, ndipo anandithandiza, chifukwa chake mtima wanga ukondwera kwakukulu; ndipo ndidzamyamika nayo nyimbo yanga.


Amitundu anagwa m'mbuna imene anaikumba, lakodwa phazi lao muukonde anautchera.