Masalimo 13:5 - Buku Lopatulika5 Koma ine ndakhulupirira pa chifundo chanu; mtima wanga udzakondwera nacho chipulumutso chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma ine ndakhulupirira pa chifundo chanu; mtima wanga udzakondwera nacho chipulumutso chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma ine ndimadalira chikondi chanu chosasinthika. Mtima wanga udzakondwera chifukwa mwandipulumutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika; mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu. Onani mutuwo |