Masalimo 116:7 - Buku Lopatulika7 Ubwere moyo wanga ku mpumulo wako; pakuti Yehova anakuchitira chokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ubwere moyo wanga ku mpumulo wako; pakuti Yehova anakuchitira chokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Iwe mtima wanga, bwerera ku malo ako opumulira, chifukwa Chauta wakuchitira zokoma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pumula iwe moyo wanga, pakuti Yehova wakuchitira zokoma. Onani mutuwo |