Masalimo 21:13 - Buku Lopatulika13 Kwezekani, Yehova, mu mphamvu yanu; potero tidzaimba ndi kulemekeza chilimbiko chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Kwezekani, Yehova, mu mphamvu yanu; potero tidzaimba ndi kulemekeza chilimbiko chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mutamandike, Inu Chauta, chifukwa cha kupambana kwanu. Tidzaimba ndi kuyamika mphamvu zanu zazikulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mukwezeke Inu Yehova mʼmphamvu yanu, ife tidzayimba nyimbo ndi kutamanda mphamvu yanu. Onani mutuwo |