Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 9:15 - Buku Lopatulika

15 Amitundu anagwa m'mbuna imene anaikumba, lakodwa phazi lao muukonde anautchera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Amitundu anagwa m'mbuna imene anaikumba, lakodwa phazi lao muukonde anautcha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Akunja agwera m'mbuna yokumba iwo omwe. Phazi lao lakodwa mu ukonde wobisika wotcha iwo omwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Mitundu ya anthu yagwa mʼdzenje limene yakumba; mapazi awo akodwa mu ukonde umene anawubisa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 9:15
11 Mawu Ofanana  

Ndipo apereke nsembe zachiyamiko, nafotokozere ntchito zake ndi kufuula mokondwera.


Ndidzaimbira Yehova, pakuti anandichitira zokoma.


Tsopano ndidziwa kuti Yehova apulumutsa wodzozedwa wake; adzamvomereza mu Mwamba mwake moyera ndi mphamvu ya chipulumutso cha dzanja lake lamanja.


Chimgwere modzidzimutsa chionongeko; ndipo ukonde wake umene anautcha umkole yekha mwini, agwemo, naonongeke m'mwemo.


Ndipo moyo wanga udzakondwera mwa Yehova; udzasekera mwa chipulumutso chake.


Lupanga lao lidzalowa m'mtima mwao momwe, ndipo mauta ao adzathyoledwa.


Ananditchera ukonde apo ndiyenda; moyo wanga wawerama. Anandikumbira mbuna patsogolo panga; anagwa m'kati mwake iwo okha.


Ndipo anawabwezera zopanda pake zao, nadzawaononga m'choipa chao; Yehova Mulungu wathu adzawaononga.


Wofesa zosalungama adzakolola tsoka; ndipo nthyole ya mkwiyo wake idzalephera.


Zoipa zakezake zidzagwira woipa; adzamangidwa ndi zingwe za uchimo wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa