Masalimo 9:16 - Buku Lopatulika16 Anadziwika Yehova, anachita kuweruza, woipayo anakodwa ndi ntchito ya manja ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Anadziwika Yehova, anachita kuweruza, woipayo anakodwa ndi ntchito ya manja ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Chauta wadziwulula yekha, pakuweruza molungama, koma anthu oipa akodwa mu msampha wotcha iwo omwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yehova amadziwika ndi chilungamo chake; oyipa akodwa ndi ntchito za manja awo. Higayoni. Sela Onani mutuwo |