Masalimo 9:17 - Buku Lopatulika17 Oipawo adzabwerera kumanda, inde amitundu onse akuiwala Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Oipawo adzabwerera kumanda, inde amitundu onse akuiwala Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Tsono anthu oipa adzapita ku dziko la anthu akufa, ndiye kuti anthu onse amene amakana Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. Onani mutuwo |