Masalimo 9:18 - Buku Lopatulika18 Pakuti sadzaiwalika nthawi zonse waumphawi, kapena chiyembekezo cha ozunzika sichidzaonongeka kosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakuti sadzaiwalika nthawi zonse waumphawi, kapena chiyembekezo cha ozunzika sichidzaonongeka kosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Koma anthu aumphaŵi Mulungu saŵaiŵala nthaŵi zonse, anthu osauka Mulungu saŵagwiritsa mwala mpang'ono pomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Koma osowa sadzayiwalika nthawi zonse, kapena chiyembekezo cha ozunzika kutayika nthawi zonse. Onani mutuwo |