Masalimo 119:7 - Buku Lopatulika7 Ndidzakuyamikani ndi mtima woongoka, pakuphunzira maweruzo anu olungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndidzakuyamikani ndi mtima woongoka, pakuphunzira maweruzo anu olungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndidzakutamandani ndikuchita zoyenera, ndikaphunzira malangizo anu olungama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndidzakutamandani ndi mtima wolungama, pamene ndikuphunzira malamulo anu olungama. Onani mutuwo |