Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 119:8 - Buku Lopatulika

8 Ndidzasamalira malemba anu: Musandisiye ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndidzasamalira malemba anu: Musandisiye ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ndidzatsata malamulo anu, musandisiye konse ndekha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ndidzamvera zophunzitsa zanu; musanditaye kwathunthu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:8
11 Mawu Ofanana  

Ndinalumbira, ndipo ndinatsimikiza mtima, kuti ndidzasamalira maweruzo anu olungama.


Ndinaitana ndi mtima wanga wonse; mundiyankhe, Yehova; ndidzasunga malemba anu.


Ndidzadzikondweretsa nao malemba anu; sindidzaiwala mau anu.


Ndinasochera ngati nkhosa yotayika; funani mtumiki wanu; pakuti sindiiwala malamulo anu.


Musanditaye kundichotsa pamaso panu; musandichotsere Mzimu wanu Woyera.


Poteronso pokalamba ine ndi kukhala nazo imvi musandisiye, Mulungu; kufikira nditalalikira mbadwo uwu za dzanja lanu, mphamvu yanu kwa onse akudza m'mbuyo.


Musanditaye mu ukalamba wanga; musandisiye, pakutha mphamvu yanga.


Ndikhoza zonse mwa Iye wondipatsa mphamvuyo.


Ndipo ngati kutumikira Yehova kukuipirani mudzisankhire lero amene mudzamtumikira, kapena milungu imene anaitumikira makolo anu okhala tsidya lija la mtsinje, kapena milungu ya Aamori amene mukhala m'dziko lao; koma ine, ndi a m'nyumba yanga, tidzatumikira Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa