Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:17 - Buku Lopatulika

Iye anatumiza kuchokera kumwamba nanditenga; Iye ananditulutsa m'madzi aakulu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iye anatumiza kuchokera kumwamba nanditenga; Iye ananditulutsa m'madzi aakulu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Ali kumwamba Chauta adatambalitsa dzanja nandigwira, ndi kundivuula m'madzi ozama.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ali kumwamba, Iye anatambalitsa dzanja lake ndipo anandigwira; anandivuwula mʼmadzi ozama.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:17
12 Mawu Ofanana  

Iye anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu, kwa iwo akudana ndi ine; pakuti anandiposa mphamvu.


M'mozamamo ndinakufuulirani, Yehova.


Tulutsani manja anu kuchokera m'mwamba; ndikwatuleni ndi kundilanditsa kumadzi aakulu, kudzanja la alendo;


Anatuma kuchokera m'mwamba, ananditenga; anandivuula m'madzi ambiri.


Chifukwa chake oyera mtima onse apemphere kwa Inu, pa nthawi ya kupeza Inu; indetu pakusefuka madzi aakulu sadzamfikira iye.


Ndipo atakula mwanayo, anapita naye kwa mwana wamkazi wa Farao, ndipo iye anakhala mwana wake. Ndipo anamutcha dzina lake Mose, nati, Chifukwa ndinamvuula m'madzi.


Pamene udulitsa pamadzi ndili pamodzi ndi iwe; ndi pooloka mitsinje sidzakukokolola; pakupyola pamoto sudzapsa; ngakhale lawi silidzakutentha.


madzi anayenda pamwamba pamutu panga, ndinati, Ndalikhidwa.


Ndipo anena ndi ine, Madziwo udawaona uko akhalako mkazi wachigololoyo ndiwo anthu, ndi makamu, ndi mitundu, ndi manenedwe.