Maliro 3:54 - Buku Lopatulika54 madzi anayenda pamwamba pamutu panga, ndinati, Ndalikhidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201454 madzi anayenda pamwamba pa mutu panga, ndinati, Ndalikhidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa54 Madzi adaamiza mutu wanga, ine nkunena ku, “Mayo, ndikufa ine!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero54 madzi anamiza mutu wanga ndipo ndinkaganiza kuti imfa yayandikira. Onani mutuwo |