Masalimo 144:7 - Buku Lopatulika7 Tulutsani manja anu kuchokera m'mwamba; ndikwatuleni ndi kundilanditsa kumadzi aakulu, kudzanja la alendo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Tulutsani manja anu kuchokera m'mwamba; ndikwatuleni ndi kundilanditsa kumadzi aakulu, kudzanja la alendo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tambasulani dzanja lanu kuchokera kumwamba. Landitseni ndi kundipulumutsa ku madzi ozama, omboleni m'manja mwa akunja, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tambasulani dzanja lanu kuchokera kumwamba; landitseni ndi kundipulumutsa, ku madzi amphamvu, mʼmanja mwa anthu achilendo, Onani mutuwo |