Masalimo 130:1 - Buku Lopatulika1 M'mozamamo ndinakufuulirani, Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 M'mozamamo ndinakufuulirani, Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndikulirira Inu Chauta, ndili m'dzenje lozama lamavuto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndikulirira kwa Inu Yehova ndili mʼdzenje lozama; Onani mutuwo |