Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 130:1 - Buku Lopatulika

1 M'mozamamo ndinakufuulirani, Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 M'mozamamo ndinakufuulirani, Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Ndikulirira Inu Chauta, ndili m'dzenje lozama lamavuto.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ndikulirira kwa Inu Yehova ndili mʼdzenje lozama;

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 130:1
22 Mawu Ofanana  

Ndikweza maso anga kumapiri: Thandizo langa lidzera kuti?


Ndinakondwera m'mene ananena nane, Tiyeni kunyumba ya Yehova.


Ndikweza maso anga kwa Inu, kwa Inu wakukhala kumwamba.


Akadapanda kukhala nafe Yehova, anene tsono Israele;


Iwo akukhulupirira Yehova akunga phiri la Ziyoni, losasunthika, likhazikika kosatha.


Pobweza Yehova ukapolo wa Ziyoni, tinakhala ngati anthu akulota.


Akapanda kumanga nyumba Yehova, akuimanga agwiritsa ntchito chabe; akapanda kusunga mzinda Yehova, mlonda adikira chabe.


Wodala yense wakuopa Yehova, wakuyenda m'njira zake.


Anandisautsa kawirikawiri kuyambira ubwana wanga, anene tsono Israele;


Anatuma kuchokera m'mwamba, ananditenga; anandivuula m'madzi ambiri.


Ndipo anandikweza kunditulutsa m'dzenje la chitayiko, ndi m'thope la pachithaphwi; nandipondetsa pathanthwe, nakhazika mayendedwe anga.


Madzi akuya aitanizana ndi madzi akuya, pa mkokomo wa matiti anu; mafunde onse a nyondonyondo anandimiza ine.


Inu, amene munationetsa nsautso zambiri ndi zoipa, mudzatipatsanso moyo, ndi kutitenganso munsi mwa dziko.


Ameneyo, m'masiku a thupi lake anapereka mapemphero ndi mapembedzero pamodzi ndi kulira kwakukulu ndi misozi kwa Iye amene anakhoza kumpulumutsa Iye muimfa, ndipo anamveka popeza anaopa Mulungu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa