Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mika 2:5 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake udzasowa woponya chingwe chamaere m'msonkhano wa Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake udzasowa woponya chingwe chamaere m'msonkhano wa Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono pa nthaŵi imene Chauta adzabwezeranso dziko kwa anthu ake, inuyo simudzalandirako gawo lililonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nʼchifukwa chake simudzakhala ndi munthu mu msonkhano wa Yehova kuti agawe dziko pochita maere.

Onani mutuwo



Mika 2:5
12 Mawu Ofanana  

mpaka Yehova adachotsa Israele pamaso pake, monga adanena mwa dzanja la atumiki ake onse aneneriwo. Momwemo Israele anachotsedwa m'dziko lao kunka nao ku Asiriya mpaka lero lino.


ndi kunena kuti, Ndidzakupatsa iwe dziko la Kanani, gawo la cholowa chako.


Ndipo okwera kuchokera ku Telemela, Teleharisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, ndi awa; koma sanakhoze kutchula nyumba za makolo ao, kapena mbumba zao, ngati ali a Israele;


Zingwe zandigwera mondikondweretsa; inde cholowa chokoma ndili nacho.


Sadzakhala m'dziko la Yehova; koma Efuremu adzabwerera kunka ku Ejipito; ndipo adzadya chakudya chodetsa mu Asiriya.


Ndipo Mose anauza ana a Israele, nati, Ili ndi dzikoli mudzalandira ndi kuchita maere, limene Yehova analamulira awapatse mafuko asanu ndi anai ndi hafu;


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Mwana wa m'chigololo asalowe m'msonkhano wa Yehova, ngakhale mbadwo wake wakhumi usalowe m'msonkhano wa Yehova.


Ana obadwa nao a mbadwo wachitatu alowe m'msonkhano wa Yehova.


Pamene Wam'mwambamwamba anagawira amitundu cholowa chao, pamene anagawa ana a anthu, anaika malire a mitundu ya anthu, monga mwa kuwerenga kwao kwa ana a Israele.


Ndipo Yoswa anawalotera maere ku Silo pamaso pa Yehova; ndi apo Yoswa anawagawira ana a Israele dziko, monga mwa magawo ao.


Mudzifunire amuna, fuko lililonse amuna atatu; kuti ndiwatume, anyamuke, nayendeyende iwo pakati padziko, nalilembe monga mwa cholowa chao; nabwerenso kwa ine.