Hoseya 9:3 - Buku Lopatulika3 Sadzakhala m'dziko la Yehova; koma Efuremu adzabwerera kunka ku Ejipito; ndipo adzadya chakudya chodetsa mu Asiriya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Sadzakhala m'dziko la Yehova; koma Efuremu adzabwerera kunka ku Ejipito; ndipo adzadya chakudya chodetsa m'Asiriya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Simudzakhalanso m'dziko la Chauta. Aefuremu inu, mudzabwerera ku ukapolo ku Ejipito, mudzadya chakudya choletsedwa ku dziko la Asiriya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Sadzakhalanso mʼdziko la Yehova. Efereimu adzabwerera ku Igupto ndipo mudzadya chakudya chodetsedwa ku Asiriya. Onani mutuwo |