Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Hoseya 9:2 - Buku Lopatulika

2 Dwale ndi choponderamo mphesa sizidzawadyetsa, vinyo watsopano adzamsowa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Dwale ndi choponderamo mphesa sizidzawadyetsa, vinyo watsopano adzamsowa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Tirigu ndi mphesa simudzakhala nazo zokwanira. Mudzasoŵanso vinyo woti muzimwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Malo opunthira tirigu ndi malo opsinyira mphesa sadzadyetsa anthu; adzasowa vinyo watsopano.

Onani mutuwo Koperani




Hoseya 9:2
12 Mawu Ofanana  

Ndipo anafika pa dwale la Atadi, lili tsidya lija la Yordani, pamenepo anamlira maliro a atate wake masiku asanu ndi limodzi.


Ndidzaleketsanso kusekerera kwake konse, zikondwerero zake, pokhala mwezi pake, ndi masabata ake, ndi misonkhano yake yonse yoikika.


Ndipo ndidzapasula mipesa yake ndi mikuyu yake, imene adanena, Iyi ndi mphotho yanga anandipatsa ondikondawo; ndipo ndidzaisandutsa thengo, ndi nyama zakuthengo zidzaidya.


Chifukwa chake ndidzabwera ndi kuchotsa tirigu wanga m'nyengo yake, ndi vinyo wanga m'nthawi yake yoikika, ndi kukwatula ubweya wanga ndi thonje langa, zimene zikadafunda umaliseche wake.


Popeza tsono mupondereza aumphawi, ndi kumsonkhetsa tirigu; mwamanga nyumba za miyala yosema, koma simudzakhala m'mwemo; mwaoka minda ya mipesa yokonda, koma simudzamwa vinyo wake.


Munayembekezera zambiri, koma taonani, pang'ono; ndipo, mutabwera napo kwanu, ndinauzirapo. Chifukwa ninji? Ati Yehova wa makamu. Chifukwa cha nyumba yanga yokhala yopasuka, ndipo nuthamangira yense kunyumba kwake.


pamenepo ponse munthu akadza ku mulu woyenera miyeso makumi awiri, pali khumi yokha; munthu akadza ku choponderamo mphesa kudzatunga mbiya makumi asanu, pali makumi awiri okha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa