Mika 2:4 - Buku Lopatulika4 Tsiku ilo adzanena fanizo lakunena inu, nadzalira maliro olemerera, ndi kuti, Tapasuka konse; iye asintha gawo la anthu anga; ha! Andichotsera ili! Agawira opikisana minda yathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Tsiku ilo adzanena fanizo lakunena inu, nadzalira maliro olemerera, ndi kuti, Tapasuka konse; iye asintha gawo la anthu anga; ha! Andichotsera ili! Agawira opikisana minda yathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsiku limenelo anthu adzakupekerani nthano yokunyodolani, adzakuimbani nyimbo yamaliro, adzati, ‘Taonongeka kotheratu. Dziko limene Chauta adatigaŵira, bwanji afuna kutilanda! Minda yathu aigaŵira amene atigwira ukapolo.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsiku limenelo anthu adzakuchitani chipongwe; adzakunyogodolani ndi nyimbo iyi yamaliro: ‘Tawonongeka kotheratu; dziko la anthu anga lagawidwa. Iye wandilanda! Wapereka minda yathu kwa anthu otiwukira.’ ” Onani mutuwo |