Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 86:3 - Buku Lopatulika

Mundichitire chifundo, Ambuye; pakuti tsiku lonse ndiitana Inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mundichitire chifundo, Ambuye; pakuti tsiku lonse ndiitana Inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mundikomere mtima, Inu Ambuye, popeza kuti ndimalirira Inu tsiku lonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mundichitire chifundo, Inu Ambuye, pakuti ndikuyitana Inu tsiku lonse.

Onani mutuwo



Masalimo 86:3
13 Mawu Ofanana  

Munditsogolere m'choonadi chanu, ndipo mundiphunzitse; pakuti Inu ndinu Mulungu wa chipulumutso changa; Inu ndikuyembekezerani tsiku lonseli.


Pakufuula ine mundiyankhe, Mulungu wa chilungamo changa; pondichepera mwandikulitsira malo. Ndichitireni chifundo, imvani pemphero langa.


Adani anga andinenera choipa, ndi kuti, adzafa liti, ndi kutayika dzina lake?


Madzulo, m'mawa, ndi msana ndidzadandaula, ndi kubuula, ndipo adzamva mau anga.


Mundichitire chifundo, Mulungu, pakuti anthu afuna kundimeza. Andipsinja pondithira nkhondo tsiku lonse.


Mundichitire chifundo, Mulungu, mundichitire chifundo; pakuti moyo wanga ukhulupirira Inu, ndipo ndithawira kumthunzi wa mapiko anu, kufikira zosakazazo zidzapita.


Kodi mudzachitira akufa zodabwitsa? Kodi adzaukanso otisiyawo, ndi kukulemekezani?


Pemphero langa lidze pamaso panu; munditcherere khutu kukuwa kwanga.


Diso langa lapuwala chifukwa cha kuzunzika kwanga: Ndimaitana Inu, Yehova, tsiku lonse; nditambalitsira manja anga kwa Inu.


Ndipo kodi Mulungu sadzachitira chilungamo osankhidwa ake akumuitana usana ndi usiku, popeza aleza nao mtima?


zaka zisanu ndi ziwiri, ndipo anali wamasiye wa kufikira zaka zake makumi asanu ndi atatu mphambu zinai, amene sankachoka ku Kachisi, wotumikira Mulungu ndi kusala kudya ndi kupemphera usiku ndi usana.


mwa pemphero lonse ndi pembedzero mupemphere nthawi yonse mwa Mzimu, ndipo pochezera pamenepo chichezerere ndi kupembedzera oyera mtima onse,