Masalimo 56:1 - Buku Lopatulika1 Mundichitire chifundo, Mulungu, pakuti anthu afuna kundimeza. Andipsinja pondithira nkhondo tsiku lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mundichitire chifundo, Mulungu, pakuti anthu afuna kundimeza. Andipsinja pondithira nkhondo tsiku lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Mulungu, mundichitire chifundo, pakuti anthu akundizunza. Adani akundithira nkhondo ndi kundipsinja tsiku lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mundichitire chifundo Inu Mulungu, pakuti anthu akundithamangitsa kwambiri; tsiku lonse akundithira nkhondo. Onani mutuwo |