Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 88:10 - Buku Lopatulika

10 Kodi mudzachitira akufa zodabwitsa? Kodi adzaukanso otisiyawo, ndi kukulemekezani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Kodi mudzachitira akufa zodabwitsa? Kodi adzaukanso otisiyawo, ndi kukulemekezani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Kodi zodabwitsa mumachitira anthu akufa? Kodi iwowo nkuuka kuti akutamandeni?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kodi mumaonetsa zozizwitsa zanu kwa anthu akufa? Kodi iwo amene afa amaukanso ndi kutamanda Inu? Sela

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 88:10
13 Mawu Ofanana  

Akufa salemekeza Yehova, kapena aliyense wakutsikira kuli chete:


Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo, ndipo ndidzafotokozera ntchito za Yehova.


Nditambalitsira manja anga kwa Inu: Moyo wanga ulira Inu monga dziko lolira mvula.


M'mwazi mwanga muli phindu lanji, potsikira ine kudzenje? Ngati fumbi lidzayamika Inu? Ngati lidzalalikira choonadi chanu?


Pakuti muimfa m'mosakumbukira Inu; m'mandamo adzakuyamikani ndani?


Mundichitire chifundo, Ambuye; pakuti tsiku lonse ndiitana Inu.


Akufa anu adzakhala ndi moyo; mitembo yao idzauka. Ukani muimbe, inu amene mukhala m'fumbi; chifukwa mame ako akunga mame a pamasamba, ndipo dziko lapansi lidzatulutsa mizimu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa