Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 41:5 - Buku Lopatulika

5 Adani anga andinenera choipa, ndi kuti, adzafa liti, ndi kutayika dzina lake?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Adani anga andinenera choipa, ndi kuti, adzafa liti, ndi kutayika dzina lake?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Koma adani anga ondifunira zoipa, amati, “Kodi munthu ameneyu adzafa liti, kuti aiŵalike?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Adani anga mwankhwidzi amanena za ine kuti, “Kodi munthu ameneyu adzafa liti kuti ayiwalike?”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 41:5
13 Mawu Ofanana  

Chikumbukiro chake chidzatayika m'dziko, ndipo adzasowa dzina kukhwalala.


koma adzatayika kosatha ngati zonyansa zake; iwo amene adamuona adzati, Ali kuti iye?


Adani anga anditonza tsiku lonse; akundiyalukirawo alumbirira ine.


Ndipo anditchera misampha iwo akufuna moyo wanga; ndipo iwo akuyesa kundichitira choipa alankhula zoononga, nalingirira zonyenga tsiku lonse.


Chifukwa ndazindikira machimo anga; ndipo choipa changa chili pamaso panga chikhalire.


Onani, Inu mukondwera ndi zoonadi m'malo a m'katimo; ndipo m'malo a m'tseri mudzandidziwitsa nzeru.


Adani anga afuna kundimeza tsiku lonse, pakuti ambiri andithira nkhondo modzikuza.


Ndidzafuulira kwa Mulungu Wam'mwambamwamba; ndiye Mulungu wonditsirizira zonse.


kuti njira yanu idziwike padziko lapansi, chipulumutso chanu mwa amitundu onse.


Mundibwerere ine, ndi kundichitira chifundo; mpatseni mtumiki wanu mphamvu yanu, ndipo pulumutsani mwana wa mdzakazi wanu.


Mundichitire chifundo, Ambuye; pakuti tsiku lonse ndiitana Inu.


Amayesa wolungama wodala pomkumbukira; koma dzina la oipa lidzavunda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa