Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 41:4 - Buku Lopatulika

4 Ndinati ine, Mundichitire chifundo, Yehova; Chiritsani mtima wanga; pakuti ndachimwira Inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndinati ine, Mundichitire chifundo, Yehova; Chiritsani mtima wanga; pakuti ndachimwira Inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono ndidati, “Inu Chauta, ndakuchimwirani, mundikomere mtima, muchiritse moyo wanga.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ndinati, “Inu Yehova, mundichitire chifundo; chiritseni pakuti ndakuchimwirani.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 41:4
8 Mawu Ofanana  

Amene akhululukira mphulupulu zako zonse; nachiritsa nthenda zako zonse;


Achiritsa osweka mtima, namanga mabala ao.


Ndinavomera choipa changa kwa Inu; ndipo mphulupulu yanga sindinaibise. Ndinati, Ndidzaululira Yehova machimo anga; ndipo munakhululukira choipa cha kulakwa kwanga.


Tiyeni, tibwerere kunka kwa Yehova; pakuti wang'amba, nadzatipoletsera; wakantha, nadzatimanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa