Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 88:2 - Buku Lopatulika

2 Pemphero langa lidze pamaso panu; munditcherere khutu kukuwa kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Pemphero langa lidze pamaso panu; munditcherere khutu kukuwa kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Pemphero langa lifike kwa Inu, tcherani khutu kuti mumve kulira kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Pemphero langa lifike pamaso panu; tcherani khutu lanu kuti mumve kulira kwanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 88:2
8 Mawu Ofanana  

Ngati munthu akachimwira mnzake, ndi lumbiro likaikidwa pa iye kumlumbiritsa, ndipo akadzalumbira patsogolo pa guwa la nsembe lanu m'nyumba ino;


Ndinafuula kusanake: ndinayembekezera mau anu.


Koma Inu ndinu woyera, wakukhala m'malemekezo a Israele.


Munditcherere khutu lanu; ndipulumutseni msanga. Mundikhalire ine thanthwe lolimba, nyumba yamalinga yakundisunga.


Kubuula kwa wandende kufike kuli Inu; monga mwa mphamvu yanu yaikulu lolani ana a imfa atsale.


Mundichitire chifundo, Ambuye; pakuti tsiku lonse ndiitana Inu.


Inde, pofuula ine ndi kuitana andithandize amakaniza pemphero langa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa