Masalimo 88:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti mzimu wanga wadzala nao mavuto, ndi moyo wanga wayandikira kumanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti mzimu wanga wadzala nao mavuto, ndi moyo wanga wayandikira kumanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pakuti mtima wanga ndi wodzaza ndi mavuto, moyo wanga ukuyandikira ku malo a anthu akufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. Onani mutuwo |