Masalimo 88:4 - Buku Lopatulika4 Anandiwerenga pamodzi nao otsikira kudzenje; ndakhala ngati munthu wopanda mphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Anandiwerenga pamodzi nao otsikira kudzenje; ndakhala ngati munthu wopanda mphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndikuŵerengedwa pamodzi ndi anthu otsikira ku manda. Ndasanduka munthu wopanda mphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndikuwerengedwa pamodzi ndi iwo amene akutsikira ku dzenje; ndine munthu wopanda mphamvu. Onani mutuwo |