Masalimo 86:4 - Buku Lopatulika4 Kondwetsani moyo wa mtumiki wanu; pakuti ndikwezera moyo wanga kwa Inu, Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Kondwetsani moyo wa mtumiki wanu; pakuti ndikwezera moyo wanga kwa Inu, Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Sangalatsani mtima wa ine mtumiki wanu, pakuti ndikupereka mtima wanga kwa Inu Ambuye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Bweretsani chimwemwe kwa mtumiki wanu, Ambuye, pakuti ndimadalira Inu. Onani mutuwo |