Masalimo 86:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti Inu, Ambuye, ndinu wabwino, ndi wokhululukira, ndi wa chifundo chochulukira onse akuitana Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti Inu, Ambuye, ndinu wabwino, ndi wokhululukira, ndi wa chifundo chochulukira onse akuitana Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Inu Ambuye ndinu abwino, ndipo mumakhululukira anthu anu. Chikondi chanu chosasinthika ndi chachikulu kwa onse amene amakupembedzani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Inu Ambuye, ndinu wokhululuka ndi wabwino, wodzaza ndi chikondi kwa onse amene amayitana Inu. Onani mutuwo |