Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 88:9 - Buku Lopatulika

9 Diso langa lapuwala chifukwa cha kuzunzika kwanga: Ndimaitana Inu, Yehova, tsiku lonse; nditambalitsira manja anga kwa Inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Diso langa lapuwala chifukwa cha kuzunzika kwanga: Ndimaitana Inu, Yehova, tsiku lonse; nditambalitsira manja anga kwa Inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 M'maso mwanga mwada ndi chisoni. Tsiku ndi tsiku ndimakuitanani, Inu Chauta, Ndimakweza manja anga kwa Inu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 maso anga ada ndi chisoni. Ndimayitana Inu Yehova tsiku lililonse; ndimakweza manja anga kwa Inu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 88:9
19 Mawu Ofanana  

Ukakonzeratu mtima wako, ndi kumtambasulira Iye manja ako;


Mabwenzi anga andinyoza; koma diso langa lilirira misozi kwa Mulungu.


M'diso mwanga muchita chizirezire chifukwa cha chisoni, ndi ziwalo zanga zonse zilibe chithunzi.


Amuonetseranji kuunika munthu wa njira yobisika, amene wamtsekera Mulungu?


Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate, ndi kusakaniza chomwera changa ndi misozi,


Nditambalitsira manja anga kwa Inu: Moyo wanga ulira Inu monga dziko lolira mvula.


Mtima wanga ugundagunda, mphamvu yanga yachoka, ndipo kuunika kwa maso anga, ndi iko komwe kwandichokera.


Ndipo anditchera misampha iwo akufuna moyo wanga; ndipo iwo akuyesa kundichitira choipa alankhula zoononga, nalingirira zonyenga tsiku lonse.


Misozi yanga yakhala ngati chakudya changa, usana ndi usiku; pakunena iwo kwa ine dzuwa lonse, Mulungu wako ali kuti?


Tikadaiwala dzina la Mulungu wathu, ndi kutambasulira manja athu kwa mulungu wachilendo;


Madzulo, m'mawa, ndi msana ndidzadandaula, ndi kubuula, ndipo adzamva mau anga.


Lapuwala diso langa chifukwa cha chisoni; lakalamba chifukwa cha onse akundisautsa.


Akulu adzafumira ku Ejipito; Kusi adzafulumira kutambalitsa manja ake kwa Mulungu.


Mundichitire chifundo, Ambuye; pakuti tsiku lonse ndiitana Inu.


Yehova, Mulungu wa chipulumutso changa, ndinafuula pamaso panu usana ndi usiku.


Wanditsekereza ndi guta, sindingatuluke; walemeretsa unyolo wanga.


Ndipo anandidzera mau a Yehova, akuti.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa