Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 2:11 - Buku Lopatulika

Tumikirani Yehova ndi mantha, ndipo kondwerani ndi chinthenthe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tumikirani Yehova ndi mantha, ndipo kondwerani ndi chinthenthe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tumikirani Chauta mwamantha ndi monjenjemera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.

Onani mutuwo



Masalimo 2:11
9 Mawu Ofanana  

Ndiye Mulungu, ayenera kumuopa kwambiri mu upo wa oyera mtima, ndiye wochititsa mantha koposa onse akumzinga.


Yehova achita ufumu; dziko lapansi likondwere; zisumbu zambiri zikondwerere.


Yehova ndiye mfumu; mitundu ya anthu injenjemere; Iye akhala pakati pa akerubi; dziko lapansi ligwedezeke.


Potero, okondedwa anga, monga momwe mumvera nthawi zonse, posati pokhapokha pokhala ine ndilipo, komatu makamaka tsopano pokhala ine palibe, gwirani ntchito yake ya chipulumutso chanu ndi mantha, ndi kunthunthumira;


Penyani musakane wolankhulayo. Pakuti ngati iwowa sanapulumuke, pomkana Iye amene anawachenjeza padziko, koposatu sitidzapulumuka ife, odzipatulira kwa Iye wa Kumwamba;