Masalimo 89:7 - Buku Lopatulika7 Ndiye Mulungu, ayenera kumuopa kwambiri mu upo wa oyera mtima, ndiye wochititsa mantha koposa onse akumzinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndiye Mulungu, ayenera kumuopa kwambiri m'upo wa oyera mtima, ndiye wochititsa mantha koposa onse akumzinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mulungu ndiye amene amamuwopa mu msonkhano wa anthu oyera mtima, ndiye wamkulu ndi wolemekezeka pakati pa onse omzungulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mu msonkhano wa oyera mtima Mulungu amaopedwa kwambiri; Iye ndiye wochititsa mantha kupambana onse amene amuzungulira. Onani mutuwo |