Masalimo 2:10 - Buku Lopatulika10 Tsono, mafumu inu, chitani mwanzeru; langikani, oweruza inu a dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Tsono, mafumu inu, chitani mwanzeru; langikani, oweruza inu a dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Nchifukwa chake tsono khalani anzeru, inu mafumu. Chenjerani inu amene muli olamula dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi. Onani mutuwo |