Masalimo 2:9 - Buku Lopatulika9 Udzawathyola ndi ndodo yachitsulo; udzawaphwanya monga mbiya ya woumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Udzawathyola ndi ndodo yachitsulo; udzawaphwanya monga mbiya ya woumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Udzaŵaphwanya ndi ndodo yachitsulo, ndi kuŵatekedza zidutswazidutswa monga mbiya.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.” Onani mutuwo |