Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 8:9 - Buku Lopatulika

Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, kuti, Fanizo ili lili lotani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, kuti, Fanizo ili lili lotani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ophunzira a Yesu adamufunsa za tanthauzo la fanizoli.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ophunzira ake anamufunsa tanthauzo lake la fanizolo.

Onani mutuwo



Luka 8:9
9 Mawu Ofanana  

Tidziwe tsono, tilondole kudziwa Yehova; kutuluka kwake kwakonzekeratu ngati matanda kucha; ndipo adzatidzera ngati mvula, ngati mvula ya masika yakuthirira dziko.


Ndipo ophunzirawo anadza, nati kwa Iye, Chifukwa chanji muphiphiritsira iwo m'mafanizo?


Ndipo tsono mverani inu fanizolo la wofesa mbeu uja.


Pomwepo Iye anasiya makamuwo, nalowa m'nyumba; ndimo ophunzira ake anadza kwa Iye, nanena, Mutitanthauzire fanizo lija la namsongole wa m'munda.


Ndipo Petro anayankha nati kwa Iye, Mutifotokozere ife fanizoli.


Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo.


ndipo sanalankhule nao wopanda fanizo: koma m'tseri anatanthauzira zonse kwa ophunzira ake.


Sinditchanso inu akapolo; chifukwa kapolo sadziwa chimene mbuye wake achita; koma ndatcha inu abwenzi; chifukwa zonse zimene ndazimva kwa Atate wanga ndakudziwitsani.