Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 13:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo ophunzirawo anadza, nati kwa Iye, Chifukwa chanji muphiphiritsira iwo m'mafanizo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo ophunzirawo anadza, nati kwa Iye, Chifukwa chanji muphiphiritsira iwo m'mafanizo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Pambuyo pake ophunzira a Yesu aja adadzamufunsa kuti, “Kodi bwanji anthuŵa mumalankhula nawo m'mafanizo?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ophunzira anabwera kwa Iye ndikumufunsa kuti, “Chifukwa chiyani Inu mukuyankhula kwa anthu mʼmafanizo?”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 13:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anayankha nati, Chifukwa kwapatsidwa kwa inu kudziwa zinsinsi za Ufumu wa Kumwamba, koma sikunapatsidwe kwa iwo.


Ndipo Iye anawauzira zinthu zambiri m'mafanizo, nanena, Onani, wofesa anatuluka kukafesa mbeu.


Amene ali ndi makutu, amve.


Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo.


Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, kuti, Fanizo ili lili lotani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa