Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 13:9 - Buku Lopatulika

9 Amene ali ndi makutu, amve.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Amene ali ndi makutu, amve.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Tsono Yesu adati, “Amene ali ndi makutu, amve!”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Amene ali ndi makutu amve.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 13:9
14 Mawu Ofanana  

Amene ali ndi makutu akumva, amve.


Ndipo ophunzirawo anadza, nati kwa Iye, Chifukwa chanji muphiphiritsira iwo m'mafanizo?


Koma maso anu ali odala, chifukwa apenya; ndi makutu anu chifukwa amva.


Ngati munthu ali nao makutu akumva, amve.


Ndipo ananena, Amene ali nao makutu akumva amve.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Iye amene apambana sadzachitidwa choipa ndi imfa yachiwiri.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye wopambana, ndidzampatsa mana obisika, ndipo ndidzampatsa mwala woyera, ndi pamwalawo dzina latsopano lolembedwapo, wosalidziwa munthu aliyense koma iye wakuulandira.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye amene apambana ndidzampatsa kudya za ku mtengo wa moyo umene uli mu Paradaiso wa Mulungu.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa