Mateyu 13:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Iye anayankha nati, Chifukwa kwapatsidwa kwa inu kudziwa zinsinsi za Ufumu wa Kumwamba, koma sikunapatsidwe kwa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Iye anayankha nati, Chifukwa kwapatsidwa kwa inu kudziwa zinsinsi za Ufumu wa Kumwamba, koma sikunapatsidwa kwa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Iye adati, “Inuyo Mulungu adakuululirani zobisika zokhudza Ufumu wakumwamba. Koma enaŵa sadaŵaululire ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iye anayankha kuti, “Nzeru zakudziwa zinsinsi za ufumu wakumwamba zapatsidwa kwa inu koma osati kwa iwo. Onani mutuwo |