Luka 8:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo zina zinagwa pa nthaka yokoma, ndipo zinamera, ndi kupatsa zipatso zamakumikhumi. Pakunena Iye izi anafuula, Iye amene ali ndi makutu akumva amve. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo zina zinagwa pa nthaka yokoma, ndipo zinamera, ndi kupatsa zipatso zamakumikhumi. Pakunena Iye izi anafuula, Iye amene ali ndi makutu akumva amve. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Koma mbeu zina zidagwera pa nthaka yabwino. Zidakula nkubereka. Ngala iliyonse inali ndi njere makumi khumi.” Tsono Yesu adalankhula mokweza mau kuti, “Amene ali ndi makutu akumva, amve!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mbewu zina zinagwera pa nthaka yabwino. Zinamera ndipo zinabala mowirikiza 100 kuposa zimene zinafesedwa zija.” Atanena izi, anafuwula kuti, “Amene ali ndi makutu, amve.” Onani mutuwo |