Luka 8:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo zina zinagwa pakati pa minga; ndi mingayo inaphuka pamodzi nazo, nkuzitsamwitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo zina zinagwa pakati pa minga; ndi mingayo inaphuka pamodzi nazo, nizitsamwitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mbeu zina zidagwera pa zitsamba zaminga. Zitsambazo pokula zidalanda chakudya cha mbeu zija. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mbewu zina zinagwera pakati pa minga, zinakulira pamodzi ndi mingazo ndipo zinalepheretsa mmerawo kukula. Onani mutuwo |