Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 13:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo tsono mverani inu fanizolo la wofesa mbeu uja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo tsono mverani inu fanizolo la wofesa mbeu uja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 “Tsono inu mumvetse bwino tanthauzo lake la fanizo la munthu wofesa mbeu lija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 “Tamverani tsono zimene fanizo la wofesa litanthauza:

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 13:18
5 Mawu Ofanana  

Pomwepo Iye anasiya makamuwo, nalowa m'nyumba; ndimo ophunzira ake anadza kwa Iye, nanena, Mutitanthauzire fanizo lija la namsongole wa m'munda.


Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa