Hoseya 6:3 - Buku Lopatulika3 Tidziwe tsono, tilondole kudziwa Yehova; kutuluka kwake kwakonzekeratu ngati matanda kucha; ndipo adzatidzera ngati mvula, ngati mvula ya masika yakuthirira dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Tidziwe tsono, tilondole kudziwa Yehova; kutuluka kwake kwakonzekeratu ngati matanda kucha; ndipo adzatidzera ngati mvula, ngati mvula ya masika yakuthirira dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tiyeni tilimbikire kusamala za Chauta. Adzabwera kwa ife mosapeneka konse ngati mbandakucha. Kubwera kwake kudzakhala madalitso ngati mvula, mvula yake yachilimwe imene imakhathamiza nthaka.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tiyeni timudziwe Yehova, tiyeni tilimbike kumudziwa Iye. Adzabwera kwa ife mosakayikira konse ngati kutuluka kwa dzuwa; adzabwera kwa ife ngati mvula ya mʼchilimwe, ngati mvula ya nthawi yamphukira imene imakhathamiritsa nthaka.” Onani mutuwo |