Hoseya 6:4 - Buku Lopatulika4 Efuremu iwe, ndidzakuchitira chiyani? Yuda iwe, ndikuchitire chiyani? Pakuti kukoma mtima kwako kukunga mtambo wam'mawa ndi ngati mame akuphawa mamawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Efuremu iwe, ndidzakuchitira chiyani? Yuda iwe, ndikuchitire chiyani? Pakuti kukoma mtima kwako kukunga mtambo wam'mawa ndi ngati mame akuphawa mamawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma Chauta akuti, “Inu Aefuremu, kodi ndikuchiteni chiyani? Nanga inu Ayuda, ndikuchiteni chiyani? Chikondi chanu chimazimirira ngati nkhungu yam'maŵa, chili ngati mame okamuka msanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iwe Efereimu, kodi ndichite nawe chiyani? Kodi ndichite nawe chiyani, iwe Yuda? Chikondi chanu chili ngati nkhungu yammawa, ngati mame a mmamawa amene amakamuka msanga. Onani mutuwo |